2 Mbiri 2:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo nyumba nditi ndimangeyi ndi yaikulu; pakuti Mulungu wathu ndiye wamkulu woposa milungu yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo nyumba nditi ndimangeyi ndi yaikulu; pakuti Mulungu wathu ndiye wamkulu woposa milungu yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Nyumba imene ndimangeyo idzakhala yaikulu, pakuti Mulungu wathu ndi wamkulu kupambana milungu yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Nyumba ya Mulungu imene ndidzamange idzakhala yayikulu, chifukwa Mulungu wathu ndi wamkulu kuposa milungu ina yonse. Onani mutuwo |