2 Mbiri 19:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo anawalangiza, ndi kuti, Muzitero ndi kuopa Yehova mokhulupirika ndi mtima wangwiro. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo anawalangiza, ndi kuti, Muzitero ndi kuopa Yehova mokhulupirika ndi mtima wangwiro. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Adaŵalamula kuti, “Muzichita ntchito imeneyi moopa Chauta, mokhulupirika, ndiponso ndi mtima wonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye anawalamula kuti, “Inu mutumikire mokhulupirika ndi mtima wanu wonse moopa Yehova. Onani mutuwo |