2 Mbiri 19:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Yehosafati anakhala ku Yerusalemu, natulukiranso mwa anthu kuyambira ku Beereseba kufikira ku mapiri a Efuremu; nawabweza atsatenso Yehova Mulungu wa makolo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Yehosafati anakhala ku Yerusalemu, natulukiranso mwa anthu kuyambira ku Beereseba kufikira ku mapiri a Efuremu; nawabweza atsatenso Yehova Mulungu wa makolo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Yehosafati ankakhala ku Yerusalemu. Adayendera anthu kuchokera ku Beereseba mpaka ku dziko lamapiri la ku Efuremu, naŵabweza kwa Chauta, Mulungu wa makolo ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yehosafati anakakhala ku Yerusalemu, ndipo amayenda pakati pa anthu kuchokera ku Beeriseba mpaka ku dziko lamapiri la Efereimu ndipo anawatembenuzira kwa Yehova, Mulungu wa makolo awo. Onani mutuwo |