Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 18:6 - Buku Lopatulika

6 Koma Yehosafati anati, Kulibenso kuno mneneri wa Yehova, kuti tifunsire kwa iye?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Koma Yehosafati anati, Kulibenso kuno mneneri wa Yehova, kuti tifunsire kwa iye?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Koma Yehosafati adafunsa kuti, “Kodi pano palibe mneneri wina wa Chauta woti tipempheko nzeru?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Koma Yehosafati anafunsanso kuti, “Kodi kuno kulibe mneneri wina wa Yehova amene ife tingafunsireko?”

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 18:6
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo mfumu ya Israele anamemeza aneneri aamuna mazana anai, nanena nao, Kodi timuke kunkhondo ku Ramoti Giliyadi kapena ndileke? Ndipo anati, Kweraniko, pakuti Mulungu adzaupereka m'dzanja la mfumu.


Ndipo mfumu ya Israele inati kwa Yehosafati, Atsalanso munthu mmodzi, tifunsire Yehova kwa iye; koma ndimuda, pakuti sandinenera ine kanthu kokoma, koma zoipa nthawi zonse, ndiye Mikaya mwana wa Imila. Nati Yehosafati, Isatero mfumu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa