2 Mbiri 18:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Yehosafati anati kwa mfumu ya Israele, Funsiranitu mau a Yehova lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Yehosafati anati kwa mfumu ya Israele, Funsiranitu mau a Yehova lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Yehosafati adauza mfumu ya ku Israele kuti, “Poyamba upemphe nzeru kwa Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma Yehosafati anatinso kwa mfumu ya Israeli, “Choyamba mupemphe nzeru kwa Yehova.” Onani mutuwo |