2 Mbiri 18:3 - Buku Lopatulika3 Nati Ahabu mfumu ya Israele kwa Yehosafati mfumu ya Yuda, Mupita nane kodi ku Ramoti Giliyadi? Nayankha, nati, Monga inu momwemo ine; monga anthu anu momwemo anthu anga; tidzakhala nanu ku nkhondoyi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Nati Ahabu mfumu ya Israele kwa Yehosafati mfumu ya Yuda, Mupita nane kodi ku Ramoti Giliyadi? Nayankha, nati, Monga inu momwemo ine; monga anthu anu momwemo anthu anga; tidzakhala nanu ku nkhondoyi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndiye Ahabu mfumu ya ku Israele adafunsa Yehosafati mfumu ya ku Yuda kuti, “Kodi udzapita nane limodzi ku Ramoti-Giliyadi?” Iyeyo adayankha kuti, “Ine ndili nanu limodzi, anthu anga nganu. Ifeyo tidzakhala nanu pa nkhondo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ahabu mfumu ya Israeli anafunsa Yehosafati mfumu ya Yuda kuti, “Kodi mudzapita nane kukalimbana ndi Ramoti Giliyadi?” Yehosafati anayankha kuti, “Ine ndili ngati inu nomwe, ndi anthu anga ngati anthu anu. Ife tikhala nanu limodzi pa nkhondoyi.” Onani mutuwo |