2 Mbiri 18:1 - Buku Lopatulika1 Yehosafati tsono anali nacho chuma ndi ulemu zomchulukira, nachita chibale ndi Ahabu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehosafati tsono anali nacho chuma ndi ulemu zomchulukira, nachita chibale ndi Ahabu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yehosafati anali ndi chuma chambiri ndi ulemerero waukulu. Tsono adachita chigwirizano chaukwati ndi banja la Ahabu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsono Yehosafati anali ndi chuma chambiri ndi ulemu, ndipo iye anachita mgwirizano wa ukwati ndi Ahabu. Onani mutuwo |