2 Mbiri 17:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Yehosafati anakula chikulire, namanga mu Yuda nyumba zansanja, ndi mizinda ya chuma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Yehosafati anakula chikulire, namanga m'Yuda nyumba zansanja, ndi midzi ya chuma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndipo mphamvu za Yehosafati zidanka zikulirakulira. Ku Yuda adamanga malinga ndi mizinda yosungirako zinthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mphamvu za Yehosafati zinkakulirakulira. Iye anamanga malo otetezedwa ndi mizinda yosungiramo chuma mu Yuda Onani mutuwo |