2 Mbiri 17:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yehosafati mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake, nadzilimbitsa kuyambana ndi Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yehosafati mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake, nadzilimbitsa kuyambana ndi Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yehosafati, mwana wa Asa, adaloŵa ufumu m'malo mwa bambo wake, ndipo adadzilimbitsa pofuna kulimbana ndi Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehosafati mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake ndipo anadzilimbitsa pofuna kulimbana ndi Israeli. Onani mutuwo |