2 Mbiri 16:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Benihadadi anamvera mfumu Asa natumiza akazembe a magulu ake a nkhondo ayambane ndi mizinda ya Israele, nakantha Iyoni, ndi Dani, ndi Abele-Maimu, ndi mizinda yonse ya chuma ya Nafutali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Benihadadi anamvera mfumu Asa natumiza akazembe a magulu ake a nkhondo ayambane ndi midzi ya Israele, nakantha Iyoni, ndi Dani, ndi Abele-Maimu, ndi midzi yonse ya chuma ya Nafutali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Benihadadi adamvera zimene adanena mfumu Asa zija, motero adatuma atsogoleri a magulu ake ankhondo kukathira nkhondo mizinda ya ku Israele. Adagonjetsa Iyoni, Dani, Abele-Maimu ndi mizinda yonse ya ku Nafutali yosungiramo zinthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Beni-Hadadi anagwirizana ndi mfumu Asa ndipo anatumiza olamulira nkhondo ake kukathira nkhondo mizinda ya Israeli. Iwo anagonjetsa Iyoni, Dani, Abeli-Maimu ndi mizinda yonse yosungira chuma ya Nafutali. Onani mutuwo |