Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 16:13 - Buku Lopatulika

13 Nagona Asa ndi makolo ake, namwalira atakhala mfumu zaka makumi anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Nagona Asa ndi makolo ake, namwalira atakhala mfumu zaka makumi anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Tsono adamwalira, pa chaka cha 41 cha ufumu wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ndipo mʼchaka cha 41 cha ufumu wake, Asa anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda pamodzi ndi makolo ake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 16:13
3 Mawu Ofanana  

Nagona Asa ndi makolo ake, naikidwa kwa makolo ake m'mzinda wa Davide kholo lake; ndipo Yehosafati mwana wake analowa ufumu m'malo mwake.


Ndipo Asa atakhala mfumu zaka makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu, anadwala nthenda ya mapazi, nikuladi nthendayi; koma podwala iye sanafune Yehova, koma asing'anga.


Ndipo anamuika m'manda ake adadzisemerawo m'mzinda wa Davide, namgoneka pa kama wodzala ndi zonunkhira za mitundumitundu, monga mwa makonzedwe a osakaniza; ndipo anampserezera zopsereza zambiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa