2 Mbiri 16:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo taonani, zochita Asa, zoyamba ndi zotsiriza, zalembedwa m'buku la mafumu a Yuda ndi Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo taonani, zochita Asa, zoyamba ndi zotsiriza, zalembedwa m'buku la mafumu a Yuda ndi Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono ntchito za Asa, kuyambira pa chiyambi mpaka pomaliza, zidalembedwa m'buku la Mafumu a ku Yuda ndi a ku Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ntchito zina za mfumu Asa, kuyambira pachiyambi mpaka kumapeto zalembedwa mʼbuku la mafumu a Yuda ndi Israeli. Onani mutuwo |