2 Mbiri 15:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo nthawi zija panalibe mtendere kwa iye wakutuluka, kapena kwa iye wakulowa, koma mavuto aakulu anagwera onse okhala m'maikomo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo nthawi zija panalibe mtendere kwa iye wakutuluka, kapena kwa iye wakulowa, koma mavuto aakulu anagwera onse okhala m'maikomo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pa masiku amenewo panalibe mtendere kwa munthu amene ankatuluka kapena kuloŵa, pakuti mavuto adaaŵagwera onse amene ankakhala m'makomo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Masiku amenewo sikunali kwabwino kuyenda ulendo, pakuti anthu onse okhala mʼdziko anali pa mavuto aakulu. Onani mutuwo |