Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 14:5 - Buku Lopatulika

5 Anachotsanso m'mizinda yonse ya Yuda misanje, ndi zifanizo za dzuwa; ndi ufumuwo unachita bata pamaso pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Anachotsanso m'midzi yonse ya Yuda misanje, ndi zifanizo za dzuwa; ndi ufumuwo unachita bata pamaso pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 M'mizinda yonse ya ku Yuda adaononga akachisi opembedzeramo mafano nagumula maguwa ofukizirapo lubani. Ndipo dzikolo lidakhala pa mtendere nthaŵi imene Asa ankalamulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Iye anachotsa malo opembedzera mafano ndi maguwa ofukizira lubani mu mzinda uliwonse wa mu Yuda, ndipo mu ufumu wake munali mtendere pa nthawi ya ulamuliro wake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 14:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Rehobowamu anakhala mu Yerusalemu, namanga mizinda yolimbikiramo mu Yuda.


nauza Yuda afune Yehova Mulungu wa makolo ao, ndi kuchita chilamulo ndi chowauza Iye.


Ndipo anthu anagumula maguwa a nsembe a Abaala pamaso pake; nawalikha mafano a dzuwa anakwezeka pamwamba pao; naphwanya zifanizo, ndi mafano osema, ndi mafano oyenga; nazipera, naziwaza pamanda pa iwo amene adaziphera nsembe.


Nagumula maguwa a nsembe, naperapera zifanizo ndi mafano osema, nalikha mafano a dzuwa onse m'dziko lonse la Israele, nabwerera kunka ku Yerusalemu.


Ndi maguwa anu a nsembe adzakhala opasuka, ndi zoimiritsa zanu zadzuwa zidzasweka; ndipo ndidzagwetsa ophedwa anu pamaso pa mafano anu.


Ndipo atapita masiku ambiri, Yehova atapumulitsa Israele kwa adani ao onse akuwazungulira, ndipo Yoswa adakalamba nakhala wa zaka zambiri;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa