2 Mbiri 14:4 - Buku Lopatulika4 nauza Yuda afune Yehova Mulungu wa makolo ao, ndi kuchita chilamulo ndi chowauza Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 nauza Yuda afune Yehova Mulungu wa makolo ao, ndi kuchita chilamulo ndi chowauza Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndipo adalamula anthu a ku Yuda kuti azitembenukira kwa Chauta, Mulungu wa makolo ao, ndi kumamvera malangizo ndi malamulo ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Asa analamula Yuda kuti afunefune Yehova Mulungu wa makolo awo ndi kumvera malamulo ndi zolamulira zake. Onani mutuwo |