2 Mbiri 14:3 - Buku Lopatulika3 nachotsa maguwa a nsembe achilendo, ndi misanje; naphwanya zoimiritsa zao, nalikha zifanizo zao, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nachotsa maguwa a nsembe achilendo, ndi misanje; naphwanya zoimiritsa zao, nalikha zifanizo zao, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adagwetsa maguwa achilendo, nkuwononga akachisi ku zitunda, nagumula zipilala zamiyala zachipembedzo, nkugwetsa mafano a Asera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iye anachotsa maguwa achilendo ndi malo opembedzerapo mafano, anaphwanya zipilala za miyala yachipembedzo ndi kugwetsa mafano a Asera. Onani mutuwo |