Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 14:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo Asa anachita chokoma ndi choyenera m'maso mwa Yehova Mulungu wake,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo Asa anachita chokoma ndi choyenera m'maso mwa Yehova Mulungu wake,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Asa adachita zokoma ndi zolungama pamaso pa Chauta, Mulungu wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Asa anachita zabwino ndi zolungama pamaso pa Yehova Mulungu wake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 14:2
15 Mawu Ofanana  

Ndipo Asa anachita zabwino pamaso pa Yehova monga Davide kholo lake.


Nachotsa m'dziko anyamata aja adama, nachotsanso mafano onse anawapanga atate ake.


Koma misanje sanaichotse, koma mtima wa Asa unali wangwiro ndi Yehova masiku ake onse.


Momwemo Abiya anagona ndi makolo ake, ndipo anamuika m'mzinda wa Davide; ndi Asa mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake; m'masiku ake dziko linaona bata zaka khumi.


nachotsa maguwa a nsembe achilendo, ndi misanje; naphwanya zoimiritsa zao, nalikha zifanizo zao,


Maaka yemwe, mai wake wa Asa, mfumu, namchotsa uyu asakhalenso mai wa ufumu, popeza anapanga fanizo lolaula; ndipo Asa analikha fanizolo, naliphwanyaphwanya, nalitenthera ku mtsinje wa Kidroni.


Ndi mtima wake unakwezeka m'njira za Yehova; anachotsanso misanje ndi zifanizo mu Yuda.


Ndipo anayenda m'njira ya Asa atate wake osapatukamo, nachita zoongoka pamaso pa Yehova.


Ndipo anamdzera kalata yofuma kwa Eliya mneneri, ndi kuti, Atero Yehova Mulungu wa Davide atate wanu, Popeza simunayende m'njira za Yehosafati atate wanu, kapena m'njira za Asa mfumu ya Yuda,


Chitatha ichi chonse tsono, Aisraele onse opezekako anatuluka kunka kumizinda ya Yuda, naphwanya zoimiritsa, nalikha zifanizo, nagamula misanje ndi maguwa a nsembe mu Yuda monse, ndi mu Benjamini, mu Efuremunso, ndi mu Manase, mpaka adaziononga zonse. Pamenepo ana onse a Israele anabwerera, yense kudziko lake ndi kumizinda yao.


Momwemo anachita Hezekiya mwa Yuda lonse nachita chokoma, ndi choyenera, ndi chokhulupirika, pamaso pa Yehova Mulungu wake.


Nagumula maguwa a nsembe, naperapera zifanizo ndi mafano osema, nalikha mafano a dzuwa onse m'dziko lonse la Israele, nabwerera kunka ku Yerusalemu.


Usagwadira milungu yao, kapena kuwatumikira, kapena kuchita monga mwa ntchito zao; koma uwapasule konse, ndi kugamulatu zoimiritsa zao.


m'chiyero ndi chilungamo pamaso pake, masiku athu onse.


nimugumule maguwa ao a nsembe, ndi kuphwanya zoimiritsa zao, ndi kutentha zifanizo zao, ndi kulikha mafano osema a milungu yao; ndipo muononge dzina lao lichoke m'malomo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa