Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 13:6 - Buku Lopatulika

6 Koma Yerobowamu mwana wa Nebati mnyamata wa Solomoni mwana wa Davide anauka, napandukana ndi mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Koma Yerobowamu mwana wa Nebati mnyamata wa Solomoni mwana wa Davide anauka, napandukana ndi mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Komabe Yerobowamu mwana wa Nebati, mtumiki wa Solomoni mwana wa Davide, adanyamuka naukira mbuyakeyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Komabe Yeroboamu mwana wa Nebati, mtumiki wa Solomoni mwana wa Davide, anawukira mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 13:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yerobowamu mwana wa Nebati Mwefuremu wa ku Zereda mnyamata wa Solomoni, dzina la amake ndiye Zeruya, mkazi wamasiye, iyenso anakweza dzanja lake pa mfumu.


Ndipo kunali, atamva Aisraele onse kuti Yerobowamu wabweranso, anatuma kumuitanira iye kumsonkhano, namlonga iye mfumu ya Aisraele onse; palibe munthu anatsata nyumba ya Davide koma fuko lokha la Yuda.


Anthu awa akamakwera kukapereka nsembe m'nyumba ya Yehova mu Yerusalemu, pamenepo mitima ya anthu awa idzatembenukiranso kwa mbuye wao, kwa Rehobowamu mfumu ya Yuda; ndipo adzandipha, nadzabweranso kwa Rehobowamu mfumu ya Yuda.


Ndipo Yehova anali naye, nachita iye mwanzeru kulikonse anamukako, napandukira mfumu ya Asiriya osamtumikira.


Motero Israele anapandukana nayo nyumba ya Davide mpaka lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa