2 Mbiri 13:6 - Buku Lopatulika6 Koma Yerobowamu mwana wa Nebati mnyamata wa Solomoni mwana wa Davide anauka, napandukana ndi mbuye wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma Yerobowamu mwana wa Nebati mnyamata wa Solomoni mwana wa Davide anauka, napandukana ndi mbuye wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Komabe Yerobowamu mwana wa Nebati, mtumiki wa Solomoni mwana wa Davide, adanyamuka naukira mbuyakeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Komabe Yeroboamu mwana wa Nebati, mtumiki wa Solomoni mwana wa Davide, anawukira mbuye wake. Onani mutuwo |