2 Mbiri 13:5 - Buku Lopatulika5 simudziwa kodi kuti Yehova Mulungu wa Israele anapereka chiperekere ufumu wa Israele kwa Davide, kwa iye ndi ana ake, ndi pangano lamchere? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 simudziwa kodi kuti Yehova Mulungu wa Israele anapereka chiperekere ufumu wa Israele kwa Davide, kwa iye ndi ana ake, ndi pangano lamchere? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kodi simukudziŵa kuti Chauta, Mulungu wa Israele, adapereka ufumu wa Israele kwa Davide ndi kwa ana ake mpaka muyaya, pochita chipangano chosaphwanyika? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kodi inu simukudziwa kuti Yehova, Mulungu wa Israeli, wapereka ufumu wa Israeli kwa Davide ndi zidzukulu zake mpaka muyaya ndiponso pangano la mchere? Onani mutuwo |