Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 13:22 - Buku Lopatulika

22 Machitidwe ena tsono a Abiya, ndi mayendedwe ake, ndi mau ake, alembedwa m'buku lomasulira la mneneri Ido.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Machitidwe ena tsono a Abiya, ndi mayendedwe ake, ndi mau ake, alembedwa m'buku lomasulira la mneneri Ido.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Ntchito zonse za Abiya, makhalidwe ake ndi zimene ankalankhula zidalembedwa m'buku la mbiri ya mneneri Ido.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Zina ndi zina zokhudza Abiya, zimene anachita ndi zimene anayankhula, zinalembedwa mʼbuku la mbiri ya mneneri Ido.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 13:22
4 Mawu Ofanana  

Machitidwe ake tsono a Rehobowamu, zoyamba ndi zotsiriza, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a Semaya mneneriyo, ndi la Ido mlauliyo, lakunena za zibadwidwe? Ndipo panali nkhondo pakati pa Rehobowamu ndi Yerobowamu masiku onse.


Koma Abiya anakula mphamvu, nadzitengera akazi khumi ndi anai, nabala ana aamuna makumi awiri mphambu awiri, ndi ana aakazi khumi mphamvu asanu ndi mmodzi.


Za ana ake tsono, ndi katundu wamkulu anamsenza, ndi kumanganso kwa nyumba ya Mulungu, taonani, zilembedwa m'buku lomasulira la mafumu. Ndipo Amaziya mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Machitidwe ena tsono a Solomoni, oyamba ndi otsiriza, sanalembedwe kodi m'buku la mau a Natani mneneri ndi m'zonenera za Ahiya wa ku Silo, ndi m'masomphenya a Ido mlauli za Yerobowamu mwana wa Nebati?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa