2 Mbiri 13:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo ana a Israele anathawa pamaso pa Yuda, nawapereka Mulungu m'dzanja lao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo ana a Israele anathawa pamaso pa Yuda, nawapereka Mulungu m'dzanja lao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Aisraele adathaŵa Ayuda, ndipo Mulungu adapereka Aisraelewo kwa Ayuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Aisraeli anathawa Ayuda. Ndipo Mulungu anawapereka mʼmanja mwawo. Onani mutuwo |