2 Mbiri 13:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo chaka chakhumi mphambu zisanu ndi zitatu cha Yerobowamu, Abiya analowa ufumu wa Yuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo chaka chakhumi mphambu zisanu ndi zitatu cha Yerobowamu, Abiya analowa ufumu wa Yuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pa chaka cha 18 cha ufumu wa Yerobowamu, Abiya adaloŵa ufumu wa ku Yuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mʼchaka cha 18 cha ulamuliro wa Yeroboamu, Abiya analowa ufumu wa Yuda, Onani mutuwo |