2 Mbiri 12:16 - Buku Lopatulika16 Nagona Rehobowamu ndi makolo ake, naikidwa m'mzinda wa Davide; ndipo Abiya mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Nagona Rehobowamu ndi makolo ake, naikidwa m'mudzi wa Davide; ndipo Abiya mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Rehobowamu adamwalira, naikidwa m'manda mu mzinda wa Davide. Tsono Abiya mwana wake adaloŵa ufumu m'malo mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Rehobowamu anamwalira, ndipo anayikidwa mʼmanda mu mzinda wa Davide. Ndipo mwana wake Abiya analowa ufumu mʼmalo wake. Onani mutuwo |