2 Mbiri 12:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo kunatero kuti pakulowa mfumu m'nyumba ya Yehova, anadza olindirira, nazinyamula, nazibwezanso ku chipinda cha olindirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo kunatero kuti pakulowa mfumu m'nyumba ya Yehova, anadza olindirira, nazinyamula, nazibwezanso ku chipinda cha olindirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono nthaŵi zonse mfumu ikamaloŵa m'Nyumba ya Chauta, alondawo ankatenga zishango, kenaka nkumazibwezera ku chipinda cha alonda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Nthawi ina iliyonse imene mfumu ikupita ku Nyumba ya Yehova, alonda amapita nayo atanyamula zishango, ndipo kenaka amakazibwezera ku chipinda cha alonda. Onani mutuwo |