Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 11:9 - Buku Lopatulika

9 ndi Adoraimu, ndi Lakisi, ndi Azeka,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 ndi Adoraimu, ndi Lakisi, ndi Azeka,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Adoraimu, Lakisi, Azeka,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Adoraimu, Lakisi, Azeka,

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 11:9
10 Mawu Ofanana  

ndi Zora, ndi Ayaloni, ndi Hebroni; ndiyo mizinda yamalinga ya mu Yuda ndi Benjamini.


ndi Gati, ndi Maresa, ndi Zifi,


Ndipo chipatukire Amaziya kusatsata Yehova, namchitira chiwembu mu Yerusalemu, nathawira ku Lakisi iyeyu; koma anatuma omtsatira ku Lakisi, namupha komweko.


Pambuyo pake Senakeribu mfumu ya Asiriya, akali ku Lakisi ndi mphamvu yake yonse pamodzi naye, anatuma anyamata kwa Hezekiya mfumu ya Yuda, ndi kwa Ayuda onse okhala ku Yerusalemu, ndi kuti,


pamene nkhondo ya mfumu ya ku Babiloni inamenyana ndi Yerusalemu, ndi mizinda yonse ya Yuda imene inatsala, ndi Lakisi ndi Azeka; pakuti mizinda ya Yuda yamalinga yotsala ndi imeneyi.


Ndipo kunali, pakuthawa iwo pamaso pa Israele, potsikira pa Betehoroni, Yehova anawagwetsera miyala yaikulu yochokera kumwamba mpaka pa Azeka, nafa iwo; akufa ndi miyala yamatalala anachuluka ndi iwo amene ana a Israele anawapha ndi lupanga.


Ndipo Yoswa, ndi Aisraele onse naye, anapitirira kuchokera ku Libina kunka ku Lakisi; namanga misasa, nathira nkhondo pa uwo;


Pamenepo mafumu asanu a Aamori, ndiwo mfumu ya ku Yerusalemu, mfumu ya ku Hebroni, mfumu ya ku Yaramuti, mfumu ya ku Lakisi, mfumu ya ku Egiloni anasonkhana, nakwera iwo ndi makamu ao onse namanga misasa pa Gibiyoni, nauthira nkhondo.


Yaramuti, ndi Adulamu, Soko, ndi Azeka;


Lakisi ndi Bozikati ndi Egiloni;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa