Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 11:8 - Buku Lopatulika

8 ndi Gati, ndi Maresa, ndi Zifi,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 ndi Gati, ndi Maresa, ndi Zifi,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Gati, Maresa, Zifi,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Gati, Maresa, Zifi,

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 11:8
13 Mawu Ofanana  

Ndipo zitatha izi, Davide anakantha Afilisti, nawagonjetsa, nalanda Gati ndi midzi yake m'manja a Afilisti.


ndi Betezuri, ndi Soko, ndi Adulamu,


ndi Adoraimu, ndi Lakisi, ndi Azeka,


Ndipo Asa anali nao ankhondo ogwira zikopa ndi mikondo, a mu Yuda zikwi mazana atatu; ndi a mu Benjamini ogwira malihawo ndi okoka mauta zikwi mazana awiri mphambu makumi asanu ndi atatu; onsewo ngwazi zamphamvu.


Ndipo anawatulukira Zera Mkusi ndi ankhondo zikwi chikwi chimodzi, ndi magaleta mazana atatu; nafika iye ku Maresa.


Pamenepo Eliyezere mwana wa Dodavahu wa Maresa ananenera kumtsutsa Yehosafati, ndi kuti, Popeza waphatikana ndi Ahaziya Yehova wapasula ntchito zako. Ndipo zombo zinasweka zosakhoza kumuka ku Tarisisi.


popeza anatuluka, nayambana ndi Afilisti, nagamula linga la Gati, ndi linga la Yabine, ndi linga la Asidodi; namanga mizinda m'dziko la Asidodi, ndi mwa Afilisti.


Ndipulumutseni, Mulungu, mwa dzina lanu, ndipo mundiweruze ndi mphamvu yanu.


Zifi ndi Telemu ndi Bealoti;


ndi Keila ndi Akizibu, ndi Maresa; mizinda isanu ndi inai pamodzi ndi midzi yao.


Maoni, Karimele, ndi Zifi, ndi Yuta;


Ndipo Davide anakhala m'chipululu m'ngaka, nakhala m'dziko la mapiri m'chipululu cha Zifi. Ndipo Saulo anamfunafuna masiku onse, koma Mulungu sadampereke m'dzanja lake.


Ndipo a ku Zifi anakwera kwa Saulo ku Gibea, nati, Davide salikubisala kwathu kodi, m'ngaka za m'nkhalango ku Horesi, m'phiri la Hakila, limene lili kumwera kwa chipululu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa