Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 11:7 - Buku Lopatulika

7 ndi Betezuri, ndi Soko, ndi Adulamu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 ndi Betezuri, ndi Soko, ndi Adulamu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Betezuri, Soko, Adulamu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Beti Zuri, Soko, Adulamu,

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 11:7
9 Mawu Ofanana  

Ndipo atatu a mwa makamu atatu opambanawo, anatsika nafika kwa Davide nyengo ya kukolola m'phanga la ku Adulamu; ndi gulu la Afilisti linamanga zithando m'chigwa cha Refaimu.


Anamangadi Betelehemu, ndi Etamu, ndi Tekowa,


ndi Gati, ndi Maresa, ndi Zifi,


Afilisti omwe adagwa m'mizinda ya kuchidikha, ndi ya kumwera kwa Yuda, nalanda Betesemesi, ndi Ayaloni, ndi Gederoti, ndi Soko ndi midzi yake, ndi Timna ndi midzi yake, ndi Gimizo ndi midzi yake; nakhala iwo komweko.


Ndidzakutengeranso wokhala mu Maresa iwe, iye amene adzakulandira ukhale cholowa chake; ulemerero wa Israele udzafikira ku Adulamu.


mfumu ya ku Libina, imodzi; mfumu ya ku Adulamu, imodzi;


Yaramuti, ndi Adulamu, Soko, ndi Azeka;


Halahulu, Betezuri, ndi Gedori,


Motero Davide anachoka kumeneko, napulumukira ku phanga la ku Adulamu; ndipo pamene abale ake ndi banja lonse la atate wake anamva, iwo anatsikira kumeneko kwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa