Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 11:6 - Buku Lopatulika

6 Anamangadi Betelehemu, ndi Etamu, ndi Tekowa,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Anamangadi Betelehemu, ndi Etamu, ndi Tekowa,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Adamanga Betelehemu, Etamu, Tekowa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Betelehemu, Etamu, Tekowa,

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 11:6
14 Mawu Ofanana  

Ndipo anafa Rakele, naikidwa panjira ya ku Efurata (ndiwo Betelehemu).


Ndipo Yowabu anatumiza ku Tekowa, natenga kumeneko mkazi wanzeru, nanena naye, Ukokomezeke monga mfedwa, nuvale zovala za pamaliro, osadzola mafuta, koma ukhale ngati munthu wamkazi wakulira akufa nthawi yaikulu.


Iwo ndiwo a atate wa Etamu: Yezireele, ndi Isima, ndi Idibasi; ndipo dzina la mlongo wao ndiye Hazeleleponi,


Etamu, ndi Aini, Rimoni, ndi Tokeni, ndi Asani, mizinda isanu;


Ndipo Rehobowamu anakhala mu Yerusalemu, namanga mizinda yolimbikiramo mu Yuda.


ndi Betezuri, ndi Soko, ndi Adulamu,


Nalawira mamawa, natuluka kunka kuchipululu cha Tekowa; ndipo potuluka iwo, Yehosafati anakhala chilili, nati, Mundimvere ine, Ayuda inu, ndi inu okhala mu Yerusalemu, limbikani mwa Yehova Mulungu wanu, ndipo mudzakhazikika; khulupirirani aneneri ake, ndipo mudzalemerera.


Potsatizana nao Atekowa anakonza gawo lina, pandunji pa nsanja yaikulu yosomphoka ndi kulinga la Ofele.


Ndi pambali pao anakonza Atekowa; koma omveka ao sanapereke makosi ao kuntchito ya Mbuye wao.


Ananu a Benjamini, pulumukani pothawa pakati pa Yerusalemu, ombani lipenga mu Tekowa, kwezani chizindikiro mu Betehakeremu; pakuti chaoneka choipa chotuluka m'mpoto ndi kuononga kwakukulu.


Mau a Amosi, amene anali mwa oweta ng'ombe a ku Tekowa, ndiwo amene anawaona za Israele masiku a Uziya mfumu ya Yuda, ndi masiku a Yerobowamu mwana wa Yowasi mfumu ya Israele, zitatsala zaka ziwiri chisanafike chivomezi.


Ndipo anawakantha nyung'unyu ndi ntchafu, makanthidwe aakulu; natsika nakhala m'phanga mwa thanthwe la ku Etamu.


Tsono Davide anali mwana wa Mwefurati uja wa ku Betelehemu ku Yuda, dzina lake ndiye Yese; ameneyu anali nao ana aamuna asanu ndi atatu; ndipo m'masiku a Saulo munthuyo anali nkhalamba, mwa anthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa