Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 11:3 - Buku Lopatulika

3 Lankhula ndi Rehobowamu mwana wa Solomoni mfumu ya Yuda ndi Benjamini, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Lankhula ndi Rehobowamu mwana wa Solomoni mfumu ya Yuda ndi Benjamini, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 “Ukauze Rehobowamu, mwana wa Solomoni, mfumu ya ku Yuda, ndi Aisraele onse a ku Yuda ndi a ku Benjamini kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 “Kawuze Rehobowamu mwana wa Solomoni mfumu ya Yuda ndi Aisraeli onse ali mu Yuda ndi Benjamini kuti,

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 11:3
8 Mawu Ofanana  

Awa onse ndiwo mafuko khumi ndi awiri a Israele: izo ndizo zomwe ananena kwa iwo atate wao nawadalitsa; yense monga mdalitso wake anawadalitsa.


Mpaka lero lino achita monga mwa miyambo yoyambayi; saopa Yehova, sachita monga mwa malemba ao, kapena maweruzo ao, kapena chilamulo, kapena choikika adachilamulira Yehova ana a Yakobo, amene anamutcha Israele,


Koma za ana a Israele okhala m'mizinda ya Yuda, Rehobowamu anakhalabe mfumu yao.


Koma mau a Yehova anadza kwa Semaya munthu wa Mulunguyo, ndi kuti,


Atero Yehova, Musamuka kukayambana ndi abale anu, bwererani yense kunyumba yake; pakuti chinthu ichi chifuma kwa Ine. Ndipo anamvera mau a Yehova, nabwerera osakayambana ndi Yerobowamu.


Ndipo Mose analembera mau onse a Yehova, nalawira kuuka mamawa, namanga guwa la nsembe patsinde paphiri, ndi zoimiritsa khumi ndi ziwiri, kwa mafuko khumi ndi awiri a Israele.


wodulidwa tsiku lachisanu ndi chitatu, wa mbadwo wa Israele, wa fuko la Benjamini, Muhebri wa mwa Ahebri; monga mwa lamulo, Mfarisi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa