2 Mbiri 11:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo anachita mwanzeru, nabalalitsa ana ake aamuna onse m'maiko onse a Yuda ndi Benjamini, kumizinda yonse yamalinga; nawapatsa chakudya chochuluka, nawafunira akazi ochuluka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo anachita mwanzeru, nabalalitsa ana ake amuna onse m'maiko onse a Yuda ndi Benjamini, kumidzi yonse yamalinga; nawapatsa chakudya chochuluka, nawafunira akazi ochuluka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Tsono mwanzeru adaika ena mwa ana ake aamuna m'zigawo zonse za ku Yuda ndi za ku Benjamini, ku mizinda yonse yamalinga. Ankaŵapatsa chakudya chambiri ndi kuŵafunira akazi ochuluka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Iye anachita mwanzeru, pomwaza ena mwa ana ake ku madera onse a Yuda ndi Benjamini, ndi ku mizinda yonse yotetezedwa. Iye anawapatsa zinthu zambiri ndiponso anawafunira akazi ambiri. Onani mutuwo |