Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 11:19 - Buku Lopatulika

19 ndipo anambalira ana, Yeusi, ndi Semariya, ndi Zahamu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 ndipo anambalira ana, Yeusi, ndi Semariya, ndi Zahamu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Mkaziyo adambalira ana aŵa: Yeusi, Semariya ndi Zahamu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Mkaziyo anamubereka ana aamuna awa: Yeusi, Semariya ndi Zahamu.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 11:19
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Rehobowamu anadzitengera mkazi Mahalati, mwana wamkazi wa Yerimoti mwana wa Davide, ndi wa Abihaili mwana wamkazi wa Eliyabu mwana wa Yese;


Ndi pambuyo pake anatenga Maaka mwana wamkazi wa Abisalomu; ndipo anambalira Abiya, ndi Atai, ndi Ziza, ndi Selomiti.


pamenepo kudzali, tsiku lakugawira ana ake aamuna chuma chake, sangakhoze kuyesa mwana wa wokondana naye woyamba kubadwa, wosati mwana wa wodana naye, ndiye woyamba kubadwatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa