Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 11:17 - Buku Lopatulika

17 Momwemo analimbikitsa ufumu wa Yuda, nalimbikitsa Rehobowamu, mwana wa Solomoni zaka zitatu; pakuti anayenda m'njira ya Davide ndi Solomoni zaka zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Momwemo analimbikitsa ufumu wa Yuda, nalimbikitsa Rehobowamu, mwana wa Solomoni zaka zitatu; pakuti anayenda m'njira ya Davide ndi Solomoni zaka zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Iwowo adalimbitsa ufumu wa Yuda, ndipo adamsunga Rehobowamu mwana wa Solomoni zaka zitatu, chifukwa chakuti pa zaka zitatuzo ankatsata chitsanzo cha Davide ndi cha Solomoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Iwo analimbikitsa ufumu wa Yuda, ndipo anathandiza Rehobowamu mwana wa Solomoni kwa zaka zitatu. Pa nthawi imeneyi iye amatsatira zochita za Davide ndi Solomoni.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 11:17
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Rehobowamu anadzitengera mkazi Mahalati, mwana wamkazi wa Yerimoti mwana wa Davide, ndi wa Abihaili mwana wamkazi wa Eliyabu mwana wa Yese;


Ndipo kunachitika, utakhazikika ufumu wa Rehobowamu, nalimbika iye, anasiya chilamulo cha Yehova, ndi Aisraele onse pamodzi naye.


Efuremu iwe, ndidzakuchitira chiyani? Yuda iwe, ndikuchitire chiyani? Pakuti kukoma mtima kwako kukunga mtambo wam'mawa ndi ngati mame akuphawa mamawa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa