2 Mbiri 11:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo akuwatsata iwo anadza ku Yerusalemu, ochokera m'mafuko onse a Israele, iwo akupereka mitima yao kufuna Yehova Mulungu wa Israele, kudzaphera Yehova Mulungu wa makolo ao nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo akuwatsata iwo anadza ku Yerusalemu, ochokera m'mafuko onse a Israele, iwo akupereka mitima yao kufuna Yehova Mulungu wa Israele, kudzaphera Yehova Mulungu wa makolo ao nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono anthu amene adatsimikiza mumtima mwao kuti azitumikira Chauta, Mulungu wa Israele, ankatsatira ansembe ndi Alevi aja, kuchoka ku mafuko a ku Israele, kupita ku Yerusalemu kukapereka nsembe kwa Chauta, Mulungu wa makolo ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Anthu ochokera fuko lililonse la Israeli amene anatsimikiza mitima yawo kufunafuna Yehova Mulungu wa Israeli, ankapitabe ku Yerusalemu kukapereka nsembe kwa Yehova, Mulungu wa makolo awo. Onani mutuwo |
Koma mukayesa dziko la cholowa chanu nchodetsa, olokani kulowa m'dziko la cholowa cha Yehova m'mene chihema cha Yehova chikhalamo, nimukhale nacho cholowa pakati pa ife; koma musapikisana ndi Yehova kapena kupikisana nafe, ndi kudzimangira nokha guwa la nsembe, pamodzi ndi guwa la nsembe la Yehova Mulungu wathu.