2 Mbiri 11:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo ansembe ndi Alevi okhala mu Israele yense anadziphatikiza kwa iye, ochokera m'malire ao onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo ansembe ndi Alevi okhala m'Israele lonse anadziphatikiza kwa iye, ochokera m'malire ao onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ansembe pamodzi ndi Alevi amene anali m'dziko lonse la Israele adatsata Rehobowamu, kuchoka konse kumene ankakhala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ansembe ndi Alevi a mʼmadera onse a Israeli anakhala mbali ya Rehobowamu. Onani mutuwo |
Koma mukayesa dziko la cholowa chanu nchodetsa, olokani kulowa m'dziko la cholowa cha Yehova m'mene chihema cha Yehova chikhalamo, nimukhale nacho cholowa pakati pa ife; koma musapikisana ndi Yehova kapena kupikisana nafe, ndi kudzimangira nokha guwa la nsembe, pamodzi ndi guwa la nsembe la Yehova Mulungu wathu.