2 Mbiri 11:12 - Buku Lopatulika12 Ndi m'mizinda iliyonse anaikamo zikopa ndi mikondo, nailimbitsa chilimbitsire. Ndipo Yuda ndi Benjamini anakhala ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndi m'midzi iliyonse anaikamo zikopa ndi mikondo, nailimbitsa chilimbitsire. Ndipo Yuda ndi Benjamini anakhala ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Adaikamo zishango ndi mikondo, ndipo adaitchinjiriza kwambiri mizindayo. Choncho ankalamulira anthu a ku Yuda ndi a ku Benjamini. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mʼmizinda yonse anayikamo zishango zikuluzikulu ndi mikondo, ndipo anachititsa kuti mizindayo ikhale yamphamvu. Choncho iye amalamulira Yuda ndi Benjamini. Onani mutuwo |