Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 11:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo analimbitsa malingawo, naikamo atsogoleri, ndi chakudya chosungikiratu, ndi mafuta, ndi vinyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo analimbitsa malingawo, naikamo atsogoleri, ndi chakudya chosungikiratu, ndi mafuta, ndi vinyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Malinga ake adamanga olimba, ndipo adaikamo atsogoleri a nkhondo. Adaikamonso chakudya, mafuta ndi vinyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Iye anakhwimitsa chitetezo cha mizindayi ndipo anayikamo atsogoleri a ankhondo, pamodzi ndi chakudya, mafuta a olivi ndi vinyo.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 11:11
7 Mawu Ofanana  

ndi Zora, ndi Ayaloni, ndi Hebroni; ndiyo mizinda yamalinga ya mu Yuda ndi Benjamini.


Ndi m'mizinda iliyonse anaikamo zikopa ndi mikondo, nailimbitsa chilimbitsire. Ndipo Yuda ndi Benjamini anakhala ake.


Ndipo anachita mwanzeru, nabalalitsa ana ake aamuna onse m'maiko onse a Yuda ndi Benjamini, kumizinda yonse yamalinga; nawapatsa chakudya chochuluka, nawafunira akazi ochuluka.


Ndipo Yehosafati anakula chikulire, namanga mu Yuda nyumba zansanja, ndi mizinda ya chuma.


Ndiwo amene analindirira mfumu, osawerenga iwo aja mfumu adawaika m'mizinda yamalinga mu Yuda monse.


Tsono, iwe wobadwa ndi munthu, Tenga mtengo umodzi, nulembepo, Wa Yuda ndi wa ana a Israele anzake; nutenge mtengo wina, nulembepo, Wa Yosefe, mtengo wa Efuremu, ndi wa nyumba yonse ya Israele anzake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa