2 Mbiri 11:10 - Buku Lopatulika10 ndi Zora, ndi Ayaloni, ndi Hebroni; ndiyo mizinda yamalinga ya mu Yuda ndi Benjamini. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndi Zora, ndi Ayaloni, ndi Hebroni; ndiyo midzi yamalinga ya m'Yuda ndi Benjamini. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Zora, Aiyaloni ndi Hebroni. Mizinda yamalinga yonseyo inali ku Yuda ndi ku Benjamini. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Zora, Ayaloni ndi Hebroni. Iyi ndiye inali mizinda yotetezedwa ya Yuda ndi Benjamini. Onani mutuwo |