2 Mbiri 10:8 - Buku Lopatulika8 Koma analeka uphungu wa akuluakuluwa adampangirawo, nakafunsana ndi anyamata anakula naye pamodzi, oimirira pamaso pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma analeka uphungu wa akulu akuluwa adampangirawo, nakafunsana ndi anyamata anakula naye pamodzi, oimirira pamaso pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Koma Rehobowamu adanyozera zimene madoda aja adaamlangiza nakapempha nzeru kwa achinyamata anzake amene adaakula naye pamodzi namamtumikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Koma Rehobowamu anakana malangizo amene akuluakulu anamupatsa ndipo anakafunsira nzeru kwa anyamata amene anakula naye pamodzi komanso amamutumikira. Onani mutuwo |