Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 10:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo ananena naye, kuti, Mukawachitira chokoma anthu awa, ndi kuwakonda, ndi kulankhula nao mau okoma, adzakhala anyamata anu kosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo ananena naye, kuti, Mukawachitira chokoma anthu awa, ndi kuwakonda, ndi kulankhula nao mau okoma, adzakhala anyamata anu kosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Madodawo adamuuza kuti, “Mukaŵachitira chifundo anthu ameneŵa ndi kumaŵasangalatsa, mukalankhula nawo mau abwino, iwowo adzakutumikirani mpaka muyaya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Iwo anayankha kuti, “Ngati inu muwakomera mtima anthu awa ndi kuwasangalatsa ndiponso kuwayankha mawu abwino, iwo adzakutumikirani nthawi zonse.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 10:7
4 Mawu Ofanana  

Nafutali ndi mbawala yomasuka; apatsa mau abwino.


Ndipo iwo anamuuza kuti, Mukakhala inu mtumiki wa anthu awa lero, ndi kuwatumikira ndi kuwayankha ndi kukamba nao mau okoma, tsono iwo adzakhala chikhalire atumiki anu.


Mayankhidwe ofatsa abweza mkwiyo; koma mau owawitsa aputa msunamo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa