2 Mbiri 10:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo ananena nao, Mubwerenso atapita masiku atatu. Nachoka anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo ananena nao, Mubwerenso atapita masiku atatu. Nachoka anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Rehobowamu adaŵauza kuti, “Mukabwerenso kuno patapita masiku atatu.” Choncho anthuwo adachoka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Rehobowamu anayankha kuti, “Mukabwerenso pakapita masiku atatu.” Choncho anthuwo anachoka. Onani mutuwo |