2 Mbiri 10:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo kunali, atamva Yerobowamu mwana wa Nebati (popeza anali mu Ejipito kumene adathawira, kuthawa Solomoni mfumu), Yerobowamu anabwera kuchoka ku Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo kunali, atamva Yerobowamu mwana wa Nebati (popeza anali m'Ejipito kumene adathawira, kuthawa Solomoni mfumu), Yerobowamu anabwera kuchoka ku Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Nthaŵi imeneyo nkuti Yerobowamu, mwana wa Nebati, ali ku Ejipito, momwe adaathaŵira mfumu Solomoni muja. Tsono atamva zaufumuzo, adachokako ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yeroboamu mwana wa Nebati atamva zimenezi (Iye anali ku Igupto, kumene anapita pothawa mfumu Solomoni) anabwerako kuchokera ku Igupto. Onani mutuwo |