2 Mbiri 10:19 - Buku Lopatulika19 Motero Israele anapandukana nayo nyumba ya Davide mpaka lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Motero Israele anapandukana nayo nyumba ya Davide mpaka lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Motero Aisraele akumpoto adakhala akupandukira banja la Davide mpaka lero lino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Motero Israeli wakhala akuwukira banja la Davide mpaka lero lino. Onani mutuwo |