2 Mbiri 10:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo mfumu inawayankha mokalipa, popeza mfumu Rehobowamu analeka uphungu wa akuluakulu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo mfumu inawayankha mokalipa, popeza mfumu Rehobowamu analeka uphungu wa akuluakulu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndiye mfumuyo idaŵayankha mwankhanza. Idanyonzera malangizo a madoda aja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mfumu inawayankha mwankhanza, pokana malangizo a akuluakulu aja. Onani mutuwo |