Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mbiri 10:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo mfumu inawayankha mokalipa, popeza mfumu Rehobowamu analeka uphungu wa akuluakulu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo mfumu inawayankha mokalipa, popeza mfumu Rehobowamu analeka uphungu wa akuluakulu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Ndiye mfumuyo idaŵayankha mwankhanza. Idanyonzera malangizo a madoda aja,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mfumu inawayankha mwankhanza, pokana malangizo a akuluakulu aja.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 10:13
11 Mawu Ofanana  

kuti, Munthu mwini dziko, ananena ndi ife mwankhalwe, natiyesa ife ozonda dziko.


Ndipo Yosefe anaona abale ake, ndipo anazindikira iwo, koma anadziyesetsa kwa iwo ngati mlendo, nanena kwa iwo mwankhanza: ndipo anati kwa iwo, Mufuma kuti inu? Nati iwo, Ku dziko la Kanani kudzagula chakudya.


Tsono Yerobowamu ndi anthu onse anabwera kwa Rehobowamu tsiku lachitatu, monga mfumu idanena, ndi kuti Bweraninso kwa ine tsiku lachitatu.


nalankhula nao monga umo anampangira achinyamata, ndi kuti, Atate wanga analemeretsa goli lanu, koma ine ndidzaonjezerapo; atate wanga anakukwapulani ndi zikoti, koma ine ndidzakukwapulani ndi zinkhanira.


Koma analeka uphungu wa akuluakuluwa adampangirawo, nakafunsana ndi anyamata anakula naye pamodzi, oimirira pamaso pake.


Ndipo Farao ananena naye, Choka pano, uzichenjera usaonenso nkhope yanga; pakuti tsiku limene uonanso nkhope yanga udzafa.


Mayankhidwe ofatsa abweza mkwiyo; koma mau owawitsa aputa msunamo.


Wosauka amadandaulira; koma wolemera ayankha mwaukali.


Ukangofuna, mwananga, kusochera kusiya mau akudziwitsa, leka kumva mwambo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa