2 Mbiri 1:9 - Buku Lopatulika9 Tsopano, Yehova Mulungu, likhazikike lonjezano lanu la kwa Davide atate wanga; pakuti mwandiika mfumu ya anthu akuchuluka ngati fumbi lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Tsopano, Yehova Mulungu, likhazikike lonjezano lanu la kwa Davide atate wanga; pakuti mwandiika mfumu ya anthu akuchuluka ngati fumbi lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Inu Chauta, zimene mudalonjeza kwa bambo wanga Davide zichitikedi, pakuti mwandiika kuti ndikhale mfumu yolamulira anthu ochuluka ngati fumbi la pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Tsopano Inu Yehova Mulungu, lolani kuti lonjezo lanu kwa abambo anga Davide likwaniritsidwe, pakuti mwandiyika kukhala mfumu ya anthu anu amene ndi ochuluka ngati fumbi la pa dziko lapansi. Onani mutuwo |