Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mbiri 1:7 - Buku Lopatulika

7 Usiku womwewo Mulungu anaonekera kwa Solomoni, nati kwa iye, Pempha chomwe ndikupatse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Usiku womwewo Mulungu anaonekera kwa Solomoni, nati kwa iye, Pempha chomwe ndikupatse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Usiku umenewo Mulungu adamuwonekera Solomoni namuuza kuti, “Upemphe chilichonse chimene ufuna kuti ndikupatse.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Usiku umenewo Mulungu anaonekera kwa Solomoni ndipo anati kwa iye, “Pempha chilichonse chimene ukufuna ndipo ndidzakupatsa.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 1:7
8 Mawu Ofanana  

Yehova anaonekera kwa Solomoni nthawi yachiwiri, monga momwe adamuonekera ku Gibiyoni.


Ndipo Yesu anamyankha, nati, Ufuna kuti ndikuchitire chiyani? Ndipo wakhunguyo anati kwa Iye, Raboni, ndilandire kuona kwanga.


Ndipo tsiku limenelo simudzandifunsa kanthu. Indetu, indetu, ndinena kwa inu, Ngati mudzapempha Atate kanthu, adzakupatsani inu m'dzina langa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa