2 Mafumu 9:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ndidzalinganiza nyumba ya Ahabu ndi nyumba ya Yerobowamu mwana wa Nebati, ndi nyumba ya Baasa mwana wa Ahiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ndidzalinganiza nyumba ya Ahabu ndi nyumba ya Yerobowamu mwana wa Nebati, ndi nyumba ya Baasa mwana wa Ahiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono Chautayo adzasandutsa banja la Ahabu kuti lifanane ndi banja la Yerobowamu mwana wa Nebati, ndiponso la Baasa mwana wa Ahiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndidzachititsa kuti banja la Ahabu lifanane ndi banja la Yeroboamu mwana wa Nebati ndiponso ngati banja la Baasa mwana wa Ahiya. Onani mutuwo |