2 Mafumu 9:7 - Buku Lopatulika7 Nudzakantha nyumba ya Ahabu mbuye wako, kuti ndibwezere chilango cha mwazi wa atumiki anga aneneri, ndi mwazi wa atumiki onse a Yehova, dzanja la Yezebele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Nudzakantha nyumba ya Ahabu mbuye wako, kuti ndibwezere chilango cha mwazi wa atumiki anga aneneri, ndi mwazi wa atumiki onse a Yehova, dzanja la Yezebele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono mukakanthe banja la Ahabu mbuyanu, kuti Chautayo alipsire Yezebele, chifukwa cha aneneri ake ndiponso atumiki ena onse amene iyeyo adaŵapha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Uyenera kuwononga nyumba ya mbuye wako Ahabu ndipo ndidzabwezera imfa ya atumiki anga, aneneri ndiponso imfa ya atumiki ena onse a Yehova amene anaphedwa ndi Yezebeli. Onani mutuwo |