2 Mafumu 9:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo atalowa, anadya namwa, nati, Kampenyeni tsono mkazi wotembereredwa uyu, nimumuike; popeza ndiye mwana wa mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo atalowa, anadya namwa, nati, Kampenyeni tsono mkazi wotembereredwa uyu, nimumuike; popeza ndiye mwana wa mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Pambuyo pake Yehu adaloŵa m'nyumba yaufumu naadya ndi kumwa. Kenaka adati, “Kamtoleni mkazi wotembereredwa uja, mukamuike, pakuti ndi mwana wa mfumu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Yehu analowa mʼnyumba yaufumu ndipo anadya ndi kumwa. Kenaka iye anati, “Kamutoleni mkazi wotembereredwayo, ndipo kamuyikeni mʼmanda, popeza ndi mwana wa mfumu.” Onani mutuwo |