Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 9:23 - Buku Lopatulika

23 Natembenuza Yoramu manja ake, nathawa, nati kwa Ahaziya, Chiwembu, Ahaziya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Natembenuza Yoramu manja ake, nathawa, nati kwa Ahaziya, Chiwembu, Ahaziya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Apo Yoramu adabwevuka nathaŵa, ndipo adafuulira Ahaziya uja kuti, “Iwe Ahaziya, atiwukira anthuŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Yoramu anatembenuka, nathawa akufuwula kwa Ahaziya kuti, “Ahaziya, anthuwa atiwukira!”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 9:23
3 Mawu Ofanana  

napenya, ndipo taonani, mfumu ili chilili pachiundo, monga ankachita, ndi atsogoleri ndi amalipenga pali mfumu; nakondwerera anthu onse a m'dziko, naomba malipenga. Pamenepo Ataliya anang'amba zovala zake, nafuula Chiwembu, Chiwembu.


napenya, ndi kuona mfumu inaima pa nsanamira yake polowera; ndi atsogoleri, ndi malipenga, anali kwa mfumu; ndi anthu onse a m'dziko anakondwera, naomba amalipenga; oimbira omwe analiko ndi zoimbirazo, nalangiza poimbira cholemekeza. Pamenepo Ataliya anang'amba zovala zake, nati, Chiwembu, chiwembu.


Pamenepo adzavomereza mphulupulu zao, ndi mphulupulu za makolo ao, pochita zosakhulupirika pa Ine; ndiponso popeza anayenda motsutsana ndi Ine,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa