2 Mafumu 9:13 - Buku Lopatulika13 Nafulumira iwo, nagwira yense chofunda chake, nachiyala pokhala iye pachiunda, naomba lipenga, nati, Yehu ndiye mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Nafulumira iwo, nagwira yense chofunda chake, nachiyala pokhala iye pachiunda, naomba lipenga, nati, Yehu ndiye mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pomwepo aliyense mwa iwowo adatenga mwinjiro wake nauyala pa makwerero, kuti Yehu akhalepo, ndipo adaliza lipenga, nalengeza kuti, “Yehu ndiye mfumu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Atsogoleri aja mofulumira anatenga zofunda zawo naziyala pansi pa makwerero kuti Yehu akhalepo. Kenaka analiza lipenga, nafuwula kuti, “Yehu ndiye mfumu!” Onani mutuwo |